Luka 18:30 - Buku Lopatulika30 koma adzalandira zobwezedwa koposatu m'nthawi ino; ndipo m'nthawi ilinkudza moyo wosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 koma adzalandira zobwezedwa koposatu m'nthawi yino; ndipo m'nthawi ilinkudza moyo wosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 ameneyo pansi pompano adzalandira zonsezo mochuluka kwambiri koposa kale, kenaka kutsogoloko adzalandira moyo wosatha.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 adzalephera kulandira mowirikiza mʼmoyo uno, ndi mʼmoyo ukubwerawo, moyo wosatha.” Onani mutuwo |