Luka 18:23 - Buku Lopatulika23 Koma pakumva izi anagwidwa nacho chisoni chambiri; pakuti anali mwini chuma chambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Koma pakumva izi anagwidwa nacho chisoni chambiri; pakuti anali mwini chuma chambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Koma pamene munthu uja adamva zimenezi, adavutika mu mtima, pakuti adaali wolemera kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Atamva zimenezi, anakhumudwa kwambiri chifukwa anali munthu wachuma chambiri. Onani mutuwo |