Luka 18:21 - Buku Lopatulika21 Koma anati, Izi zonse ndazisunga kuyambira ubwana wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Koma anati, Izi zonse ndazisunga kuyambira ubwana wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Munthu uja adati, “Zonsezi ndakhala ndikuzitsata kuyambira ndili mwana.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Iye anati, “Zonsezi ndinasunga kuyambira ndili mnyamata.” Onani mutuwo |