Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 18:21 - Buku Lopatulika

21 Koma anati, Izi zonse ndazisunga kuyambira ubwana wanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Koma anati, Izi zonse ndazisunga kuyambira ubwana wanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Munthu uja adati, “Zonsezi ndakhala ndikuzitsata kuyambira ndili mwana.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Iye anati, “Zonsezi ndinasunga kuyambira ndili mnyamata.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:21
9 Mawu Ofanana  

Koma anayankha nati kwa atate wake, Onani, ine ndinakhala kapolo wanu zaka zambiri zotere, ndipo sindinalakwire lamulo lanu nthawi iliyonse; ndipo simunandipatse ine kamodzi konse mwanawambuzi, kuti ndisekere ndi abwenzi anga.


Ndinena kwa inu, kotero kudzakhala chimwemwe Kumwamba chifukwa cha wochimwa mmodzi wotembenuka mtima, koposa anthu olungama makumi asanu ndi anai mphambu asanu ndi anai, amene alibe kusowa kutembenuka mtima.


Udziwa malamulo. Usachite chigololo, Usaphe, Usabe, Usachite umboni wonama, Lemekeza atate wako ndi amai ako.


Koma m'mene Yesu anamva, anati kwa iye, Usowa chinthu chimodzi: gulitsa zilizonse uli nazo, nugawire osauka; ndipo udzakhala nacho chuma chenicheni mu Mwamba; ndipo ukadze kuno, unditsate Ine.


monga mwa changu, wolondalonda Mpingo; monga mwa chilungamo cha m'lamulo wokhala wosalakwa ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa