Luka 18:2 - Buku Lopatulika2 nanena, M'mzinda mwakuti munali woweruza wosaopa Mulungu, ndi wosasamala munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 nanena, M'mudzi mwakuti munali woweruza wosaopa Mulungu, ndi wosasamala munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adati, “M'mudzi mwina mudaali woweruza wina amene sankaopa Mulungu kapena kulabadako za munthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iye anati, “Mʼmudzi wina munali woweruza wosaopa Mulungu ngakhalenso kulabadira za anthu. Onani mutuwo |