Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 17:32 - Buku Lopatulika

32 Kumbukirani mkazi wa Loti.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Kumbukirani mkazi wa Loti.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Kumbukirani za mkazi wa Loti.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Kumbukirani mkazi wa Loti!

Onani mutuwo Koperani




Luka 17:32
6 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene anawatulutsa iwo kunja, anati, Tapulumuka ndi moyo wako; usacheuke, usakhale pachigwa paliponse; thawira kuphiri, kuti unganyeke.


Koma mkazi wake anacheuka ali pambuyo pake pa Loti, nasanduka mwala wamchere.


Iye aliyense akafuna kusunga moyo wake adzautaya, koma iye aliyense akautaya, adzausunga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa