Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 17:33 - Buku Lopatulika

33 Iye aliyense akafuna kusunga moyo wake adzautaya, koma iye aliyense akautaya, adzausunga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Iye aliyense akafuna kusunga moyo wake adzautaya, koma iye aliyense akautaya, adzausunga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Aliyense woyesa kudzisungira moyo wake, adzautaya, koma woutaya adzausunga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Aliyense amene ayesetsa kusunga moyo wake adzawutaya, ndipo aliyense amene ataya moyo wake adzawusunga.

Onani mutuwo Koperani




Luka 17:33
7 Mawu Ofanana  

Iye amene apeza moyo wake, adzautaya; ndi iye amene ataya moyo wake, chifukwa cha Ine, adzaupeza.


Pakuti iye amene afuna kupulumutsa moyo wake adzautaya: koma iye amene ataya moyo wake chifukwa cha Ine, adzaupeza.


Ndinena ndi inu, usiku womwewo adzakhala awiri pa kama mmodzi; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.


Iye wokonda moyo wake adzautaya; ndipo wodana ndi moyo wake m'dziko lino lapansi adzausungira kumoyo wosatha.


Usaope zimene uti udzamve kuwawa; taona, mdierekezi adzaponya ena a inu m'nyumba yandende, kuti mukayesedwe; ndipo mudzakhala nacho chisautso masiku khumi. Khala wokhulupirika kufikira imfa, ndipo ndidzakupatsa iwe korona wa moyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa