Luka 17:29 - Buku Lopatulika29 koma tsiku limene Loti anatuluka mu Sodomu udavumba moto ndi sulufure zochokera kumwamba, ndipo zinawaononga onsewo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 koma tsiku limene Loti anatuluka m'Sodomu udavumba moto ndi sulufure zochokera kumwamba, ndipo zinawaononga onsewo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Koma tsiku limene Loti adatuluka m'Sodomu, Mulungu adagwetsa moto ndi miyala yoyaka ya sulufule nkuŵaononga onsewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Koma tsiku limene Loti anachoka ku Sodomu, moto ndi sulufule zinavumbwa kuchokera kumwamba ndi kuwawononga onsewo. Onani mutuwo |
Chifukwa chake, pali moyo wanga, ati Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele, Zedi Mowabu adzakhala ngati Sodomu, ndi ana a Amoni ngati Gomora, pochuluka khwisa ndi maenje a mchere, ndi bwinja losatha; otsala a anthu anga adzalanda zao, ndi otsala a mtundu wa anthu anga adzawalandira akhale cholowa chao.