Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 17:23 - Buku Lopatulika

23 Ndipo adzanena ndi inu, Taonani ilo! Taonani ili? Musachoka kapena kuwatsata;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndipo adzanena ndi inu, Taonani ilo! Taonani ili? Musachoka kapena kuwatsata;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Anthu azidzakuuzani kuti, ‘Suuwo uli uko,’ kapena, ‘Suuwu uli pano,’ musadzapiteko kapena kuŵatsatira ai.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Anthu adzakuwuzani kuti, ‘Uyo ali apoyo!’ kapena ‘Uyu ali apa!’ Musawathamangire iwo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 17:23
4 Mawu Ofanana  

ndipo sadzanena, Taonani uwu, kapena uwo! Pakuti, taonani, Ufumu wa Mulungu uli m'kati mwa inu.


Ndipo Iye anati, Yang'anirani musasocheretsedwe; pakuti ambiri adzadza m'dzina langa, nadzanena, Ndine amene; ndipo, Nthawi yayandikira; musawatsate pambuyo pao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa