Luka 16:17 - Buku Lopatulika17 Kuti thambo ndi dziko lapansi zichoke nkwapafupi, koma kuti kalembo kakang'ono kachilamulo kagwe nkwapatali. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Kuti kumwamba ndi dziko lapansi zichoke nkwapafupi, koma kuti kalembo kakang'ono kachilamulo kagwe nkwapatali. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma nkwapafupi kuti thambo ndi dziko lapansi zithe, kupambana kuti kalemba kakang'ono ka pa Malamulo kathe mphamvu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Nʼkwapafupi kuti kumwamba ndi dziko lapansi zichoke kulekana ndi kuti kalemba kakangʼono kachoke mʼMalamulo. Onani mutuwo |