Luka 16:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo ngati simunakhale okhulupirika ndi zake za wina, adzakupatsani inu ndani za inu eni? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo ngati simunakhala okhulupirika ndi zake za wina, adzakupatsani inu ndani za inu eni? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ndipo ngati mwakhala osakhulupirika ndi za wina, ndani adzakupatseni zimene zili zanuzanu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndipo ngati simunakhale okhulupirika ndi chuma cha mwini wake, ndani amene adzakupatsani katundu wanuwanu? Onani mutuwo |