Luka 15:23 - Buku Lopatulika23 ndipo idzani naye mwanawang'ombe wonenepa, mumuphe, ndipo tidye, tisekere; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 ndipo idzani naye mwanawang'ombe wonenepa, mumuphe, ndipo tidye, tisekere; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Ndipo katengeni mwanawang'ombe wonenepa uja, muphe kuti tidye, tikondwere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Bweretsani mwana wangʼombe wonenepa ndipo iphani. Tiyeni tikhale ndi phwando ndi kukondwerera. Onani mutuwo |