Luka 13:31 - Buku Lopatulika31 Nthawi yomweyo anadzapo Afarisi ena, nanena kwa Iye, Tulukani, chokani kuno; chifukwa Herode afuna kupha Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Nthawi yomweyo anadzapo Afarisi ena, nanena kwa Iye, Tulukani, chokani kuno; chifukwa Herode afuna kupha Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Nthaŵi yomweyo Afarisi ena adadzauza Yesu kuti, “Muchokeko kuno, chifukwa Herode akufuna kukuphani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Pa nthawi imeneyo Afarisi anabwera kwa Yesu ndipo anati kwa Iye, “Chokani malo ano ndipo pitani kumalo ena aliwonse. Herode akufuna kukuphani.” Onani mutuwo |