Luka 13:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo anthu adzachokera kum'mawa, ndi kumadzulo, ndi kumpoto, ndi kumwera, nadzakhala pansi mu Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo anthu adzachokera kum'mawa, ndi kumadzulo, ndi kumpoto, ndi kumwera, nadzakhala pansi mu Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Anthu adzachokera kuvuma ndi kuzambwe, kumpoto ndi kumwera, nadzakhala podyera mu Ufumu wa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Anthu adzachokera kummawa ndi kumadzulo, kumpoto ndi kummwera, kudzakhala pa phwando mu ufumu wa Mulungu. Onani mutuwo |