Luka 13:27 - Buku Lopatulika27 ndipo Iye adzati, Ndinena kwa inu, sindidziwa kumene muchokera inu; chokani pa Ine, nonse akuchita chosalungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 ndipo Iye adzati, Ndinena kwa inu, sindidziwa kumene muchokera inu; chokani pa Ine, nonse akuchita chosalungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Koma Iye adzakuuzani kuti, ‘Pepani, sindikudziŵa kumene mukuchokera. Chokani apa nonsenu, anthu ochita zoipa.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 “Koma Iye adzayankha kuti, ‘Ine sindikukudziwani ndipo sindikudziwanso kumene mwachokera. Chokereni inu nonse ochita zoyipa!’ Onani mutuwo |