Luka 13:20 - Buku Lopatulika20 Ndiponso anati, Ndidzafanizira Ufumu wa Mulungu ndi chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndiponso anati, Ndidzafanizira Ufumu wa Mulungu ndi chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Yesu adatinso, “Ndingayerekezenso ndi chiyani Ufumu wa Mulungu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iye anafunsanso kuti, “Kodi ufumu wa Mulungu ndingawufanizire ndi chiyani? Onani mutuwo |