Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 13:20 - Buku Lopatulika

20 Ndiponso anati, Ndidzafanizira Ufumu wa Mulungu ndi chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndiponso anati, Ndidzafanizira Ufumu wa Mulungu ndi chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Yesu adatinso, “Ndingayerekezenso ndi chiyani Ufumu wa Mulungu?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Iye anafunsanso kuti, “Kodi ufumu wa Mulungu ndingawufanizire ndi chiyani?

Onani mutuwo Koperani




Luka 13:20
4 Mawu Ofanana  

Koma ndidzafanizira ndi chiyani obadwa awa a makono? Ali ofanana ndi ana akukhala m'mabwalo a malonda, amene alikuitana anzao.


Fanizo lina Iye anawafotokozera iwo, nanena, Ufumu wa Kumwamba ufanizidwa ndi munthu, amene anafesa mbeu zabwino m'munda mwake;


Pamenepo ananena, Ufumu wa Mulungu ufanana ndi chiyani? Ndipo ndidzaufanizira ndi chiyani?


Ufanana ndi chotupitsa mikate, chimene mkazi anatenga, nachibisa mu miyeso itatu ya ufa, kufikira unatupo wonsewo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa