Luka 12:7 - Buku Lopatulika7 komatu ngakhale matsitsi onse a pamutu panu awerengedwa. Musaopa, muposa mtengo wake wa mpheta zambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 komatu ngakhale matsitsi onse a pamutu panu awerengedwa. Musaopa, muposa mtengo wake wa mpheta zambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndipo tsitsi lomwe la kumutu kwanu adaliŵerenga lonse. Choncho musati muziwopa ai. Ndinu a mtengo woposa atimba ambiri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndithudi, tsitsi lonse la mʼmutu mwanu ndi lowerengedwa. Musachite mantha; inu ndi oposa kwambiri mpheta zambiri. Onani mutuwo |