Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 12:54 - Buku Lopatulika

54 Koma Iye ananenanso kwa makamu a anthu, Pamene paliponse muona mtambo wokwera kumadzulo, pomwepo munena, kuti, Ikudza mvula; ndipo itero.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

54 Koma Iye ananenanso kwa makamu a anthu, Pamene paliponse muona mtambo wokwera kumadzulo, pomwepo munena, kuti, Ikudza mvula; ndipo itero.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

54 Yesu adauzanso anthu onse aja kuti, “Mukaona mtambo ukukwera kuzambwe, pompo mumati, ‘Mvula ikubwera,’ ndipo imabweradi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

54 Iye anati kwa gulu la anthu, “Pamene mukuona mtambo ukukwera kummawa, nthawi yomweyo inu mumati, ‘kugwa mvula,’ ndipo imagwadi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 12:54
2 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa