Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 12:55 - Buku Lopatulika

55 Ndipo pamene mphepo ya kumwera iomba, munena, kuti, Kudzakhala kutenthatu; ndipo kuterodi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

55 Ndipo pamene mphepo ya kumwera iomba, munena, kuti, Kudzakhala kutenthatu; ndipo kuterodi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

55 Mphepo yakumwera ikamaomba, mumati, ‘Kutentha,’ ndipo kumatenthadi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

55 Ndipo pamene mphepo yakummwera ikuwomba, inu mumati ‘kutentha’ ndipo kumaterodi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 12:55
3 Mawu Ofanana  

Kodi mudziwa umo zovala zanu zifundira, pamene dziko lili thuu chifukwa cha mwera?


nati, Omalizira awa anagwira ntchito mphindi yaing'ono, ndipo munawalinganiza ndi ife amene tinapirira kuwawa kwa dzuwa ndi kutentha kwake.


Koma iwe popatsa mphatso zachifundo, dzanja lako lamanzere lisadziwe chimene lichita dzanja lako lamanja;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa