Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 12:23 - Buku Lopatulika

23 Pakuti moyo uli woposa chakudya, ndi thupi liposa chovala.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Pakuti moyo uli woposa chakudya, ndi thupi liposa chovala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Pakuti moyo umaposa chakudya, ndipo thupi limaposa zovala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Moyo uposa chakudya, ndi thupi liposa chovala.

Onani mutuwo Koperani




Luka 12:23
9 Mawu Ofanana  

Ndipo panali pamene anawatulutsa iwo kunja, anati, Tapulumuka ndi moyo wako; usacheuke, usakhale pachigwa paliponse; thawira kuphiri, kuti unganyeke.


Nati Yehova kwa Satana, Taona, zonse ali nazo zikhale m'dzanja mwako; pa iye pokha usatambasula dzanja lako. Natuluka Satana pamaso pa Yehova.


Nayankha Satana, nati kwa Yehova, Khungu kulipa khungu, inde munthu adzapereka zonse ali nazo kuombola moyo wake.


Ndipo Yehova anati kwa Satana, Taona, akhale m'dzanja lako; moyo wake wokha uuleke.


Chiombolo cha moyo wa munthu ndicho chuma chake; koma wosauka samva chidzudzulo.


Ndipo Iye anati kwa ophunzira ake, Chifukwa chake ndinena ndinu, Musade nkhawa ndi moyo wanu, chimene mudzadya; kapena ndi thupi lanu, chimene mudzavala.


Lingirirani makwangwala, kuti samafesai, kapena kutemai; alibe nyumba yosungiramo, kapena nkhokwe; ndipo Mulungu awadyetsa; nanga inu simuziposa mbalame kwambiri!


Ndipo m'mene anakhuta, anapepuza ngalawa, nataya tirigu m'nyanja.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa