Luka 12:23 - Buku Lopatulika23 Pakuti moyo uli woposa chakudya, ndi thupi liposa chovala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Pakuti moyo uli woposa chakudya, ndi thupi liposa chovala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Pakuti moyo umaposa chakudya, ndipo thupi limaposa zovala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Moyo uposa chakudya, ndi thupi liposa chovala. Onani mutuwo |