Luka 12:21 - Buku Lopatulika21 Atero iye wakudziunjikira chuma mwini yekha wosakhala nacho chuma cha kwa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Atero iye wakudziunjikira chuma mwini yekha wosakhala nacho chuma cha kwa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Potsiriza Yesu adati, “Zimatero ndi munthu amene amadziwunjikira chuma, koma sali wachuma konse pamaso pa Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 “Umu ndi mmene zidzakhalire ndi aliyense amene amadziwunjikira chuma, koma si wachuma pamaso pa Mulungu.” Onani mutuwo |