Luka 12:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo anaganizaganiza mwa yekha nanena, Ndidzatani ine, popeza ndilibe mosungiramo zipatso zanga? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo anaganizaganiza mwa yekha nanena, Ndidzatani ine, popeza ndilibe mosungiramo zipatso zanga? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ndiye iye uja adayamba kuganiza kuti, ‘Nditani, poti ndilibe mosungira dzinthu dzanga?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Iye anaganiza kuti, ‘Ndichite chiyani? Ndilibe malo osungiramo mbewu zanga.’ Onani mutuwo |