Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 11:3 - Buku Lopatulika

3 tipatseni ife tsiku ndi tsiku chakudya cha patsiku.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 tipatseni ife tsiku ndi tsiku chakudya cha patsiku.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Mutipatse ife tsiku lililonse chakudya chathu chamasikuwonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Mutipatse chakudya chathu chalero,

Onani mutuwo Koperani




Luka 11:3
7 Mawu Ofanana  

Mundichotsere kutali zachabe ndi mabodza; musandipatse umphawi, ngakhale chuma, mundidyetse zakudya zondiyenera;


iye adzakhala pamsanje; malo ake ochinjikiza adzakhala malinga amiyala; chakudya chake chidzapatsidwa kwa iye; madzi ake adzakhala chikhalire.


Mutipatse ife lero chakudya chathu chalero.


Chifukwa chake musadere nkhawa za mawa; pakuti mawa adzadzidera nkhawa iwo okha. Zikwanire tsiku zovuta zake.


Amenewa anali mfulu koposa a mu Tesalonika, popeza analandira mau ndi kufunitsa kwa mtima wonse, nasanthula m'malembo masiku onse, ngati zinthu zinali zotero.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa