Luka 10:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo anali ndi mbale wake wotchedwa Maria, ndiye wakukhala pa mapazi a Ambuye, namva mau ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo anali ndi mbale wake wotchedwa Maria, ndiye wakukhala pa mapazi a Ambuye, namva mau ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Iyeyu anali ndi mng'ono wake, dzina lake Maria, amene adaadzakhala pansi ku mapazi a Ambuye, namamva mau ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Mayiyu anali ndi mchemwali wake wotchedwa Mariya, amene anakhala pa mapazi a Yesu kumverera zimene Iye ankanena. Onani mutuwo |