Luka 1:79 - Buku Lopatulika79 Kuwalitsira iwo okhala mumdima ndi mthunzi wa imfa; kulunjikitsa mapazi athu mu njira ya mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201479 Kuwalitsira iwo okhala mumdima ndi mthunzi wa imfa; kulunjikitsa mapazi athu mu njira ya mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa79 Kuŵala kwake kudzaunikira onse okhala mu mdima wabii ngati wa imfa, kudzatitsogolera pa njira ya mtendere.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero79 kuwalira iwo okhala mu mdima ndi mu mthunzi wa imfa, kutsogolera mapazi athu mu njira yamtendere.” Onani mutuwo |