Luka 1:78 - Buku Lopatulika78 chifukwa cha mtima wachifundo wa Mulungu wathu. M'menemo mbandakucha wa kumwamba udzatichezera ife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201478 chifukwa cha mtima wachifundo wa Mulungu wathu. M'menemo mbandakucha wa kumwamba udzatichezera ife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa78 Mulungu wathu ndi wa chifundo chachikulu, adzatitumizira kuŵala kwa dzuŵa lam'maŵa kuchokera Kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero78 chifukwa cha chifundo chachikulu cha Mulungu wathu, ndipo kuwala kwa dzuwa kudzafikira ife kuchokera kumwamba, Onani mutuwo |