Luka 1:77 - Buku Lopatulika77 Kuwapatsa anthu ake adziwitse chipulumutso, ndi makhululukidwe a machimo ao, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201477 Kuwapatsa anthu ake adziwitse chipulumutso, ndi makhululukidwe a machimo ao, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa77 Udzadziŵitsa anthu ao kuti Mulungu adzaŵapulumutsa pakuŵakhululukira machimo ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero77 kupatsa anthu ake chidziwitso cha chipulumutso kudzera mwa chikhululukiro cha machimo awo, Onani mutuwo |