Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:34 - Buku Lopatulika

34 Koma Maria anati kwa mngelo, Ichi chidzachitika bwanji, popeza ine sindidziwa mwamuna?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Koma Maria anati kwa mngelo, Ichi chidzachitika bwanji, popeza ine sindidziwa mwamuna?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Koma Maria adafunsa mngeloyo kuti, “Zimenezi zidzachitika bwanji, popeza kuti sindidziŵa mwamuna?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Mariya anafunsa mngeloyo kuti, “Izi zingatheke bwanji popeza ine sindidziwa mwamuna?”

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:34
4 Mawu Ofanana  

ndipo Iye adzachita ufumu pa banja la Yakobo kunthawi zonse; ndipo ufumu wake sudzatha.


Ndipo mngelo anayankha, nati kwa iye, Mzimu Woyera adzafika pa iwe, ndi mphamvu ya Wamkulukulu idzakuphimba iwe: chifukwa chakenso Choyeracho chikadzabadwa, chidzatchedwa Mwana wa Mulungu.


komatu, uka, nulowe m'mzinda, ndipo kudzanenedwa kwa iwe chimene uyenera kuchita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa