Luka 1:33 - Buku Lopatulika33 ndipo Iye adzachita ufumu pa banja la Yakobo kunthawi zonse; ndipo ufumu wake sudzatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 ndipo Iye adzachita ufumu pa banja la Yakobo kunthawi zonse; ndipo ufumu wake sudzatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 ndipo adzakhala Mfumu ya Aisraele mpaka muyaya. Ufumu wake sudzatha konse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 ndipo adzalamulira pa nyumba ya Yakobo ku nthawi zonse; ufumu wake sudzatha.” Onani mutuwo |