Luka 1:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo pakulowa mngelo anati kwa iye, Tikuoneni, wochitidwa chisomo, Ambuye ali ndi iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo pakulowa mngelo anati kwa iye, Tikuoneni, wochitidwa chisomo, Ambuye ali ndi iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Mngelo uja adadza kwa iye nati, “Moni, inu amene Mulungu wakukomerani mtima kotheratu. Ambuye ali nanu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Mngeloyo anafika kwa iye nati, “Moni, inu amene Ambuye wakukomerani mtima kwambiri! Ambuye ali ndi inu.” Onani mutuwo |