Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo anthu analikulindira Zekariya, nazizwa ndi kuchedwa kwake mu Kachisimo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo anthu analikulindira Zekariya, nazizwa ndi kuchedwa kwake m'Kachisimo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Nthaŵi yonseyo anthu aja ankadikira Zakariya, nkumadabwa kuti akuchedwa m'Nyumba ya Mulungumo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Pa nthawiyi, anthu ankadikira Zakariya ndipo anadabwa chifukwa anatenga nthawi yayitali ali mʼNyumba ya Mulungu.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:21
5 Mawu Ofanana  

Ndipo iye anataya pansi ndalamazo pa Kachisi, nachokapo, nadzipachika yekha pakhosi.


Ndipo pakumva ichi, Yesu anazizwa, nati kwa iwo akumtsata, Indetu ndinena kwa inu, ngakhale mwa Israele, sindinapeze chikhulupiriro chotere.


Ndipo taona, udzakhala wotonthola ndi wosakhoza kulankhula, kufikira tsiku limene zidzachitika izi, popeza kuti sunakhulupirire mau anga, amene adzakwanitsidwa pa nyengo yake.


Koma m'mene iye anatulukamo, sanathe kulankhula nao; ndipo anazindikira kuti iye adaona masomphenya mu Kachisimo. Ndipo iye analinkukodola iwo, nakhalabe wosalankhula.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa