Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo iye adzatembenuzira ana a Israele ambiri kwa Ambuye Mulungu wao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo iye adzatembenuzira ana a Israele ambiri kwa Ambuye Mulungu wao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Adzatembenuza Aisraele ambiri kuti abwerere kwa Ambuye, Mulungu wao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Iye adzabweretsanso Aisraeli ambiri kwa Ambuye Mulungu wawo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:16
8 Mawu Ofanana  

inde, ati, Chili chinthu chopepuka ndithu kuti Iwe ukhale mtumiki wanga wakuutsa mafuko a Yakobo, ndi kubwezera osungika a Israele; ndidzakupatsanso ukhale kuunika kwa amitundu, kuti ukhale chipulumutso changa mpaka ku malekezero a dziko lapansi.


Ndipo aphunzitsi adzawala ngati kunyezimira kwa thambo; ndi iwo otembenuza ambiri atsate chilungamo ngati nyenyezi kunthawi za nthawi.


Taonani, ndituma mthenga wanga, kuti akonzeretu njira pamaso panga; ndipo Ambuye amene mumfuna adzadza ku Kachisi wake modzidzimutsa; ndiye mthenga wa chipangano amene mukondwera naye; taonani akudza, ati Yehova wa makamu.


Popeza Yohane anadza kwa inu m'njira ya chilungamo, ndipo simunamvere iye; koma amisonkho ndi akazi achiwerewere anammvera iye; ndipo inu, m'mene munachiona, simunalape pambuyo pake, kuti mumvere iye.


Eya, ndipo iwetu kamwanawe, udzanenedwa mneneri wa Wamkulukulu; pakuti udzatsogolera Ambuye, kukonza njira zake.


Ndipo iye anadza kudziko lonse la m'mbali mwa Yordani, nalalikira ubatizo wa kulapa mtima kuloza ku chikhululukiro cha machimo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa