Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 1:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo Zekariya anadabwa pamene anamuona, ndipo mantha anamgwira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo Zekariya anadabwa pamene anamuona, ndipo mantha anamgwira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Zakariya adadzidzimuka pomuwona, nachita mantha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Zakariya ataona mngeloyo, anadzidzimuka ndipo anagwidwa ndi mantha.

Onani mutuwo Koperani




Luka 1:12
9 Mawu Ofanana  

Ndipo ine Daniele ndekha ndinaona masomphenyawo; pakuti anthu anali nane sanaone masomphenyawo; koma kunawagwera kunjenjemera kwakukulu, nathawa kubisala.


Ndipo pamene analowa m'manda, anaona mnyamata alikukhala kumbali ya kudzanja lamanja, wovala mwinjiro woyera; ndipo iwo anadabwa.


Koma iye ananthunthumira ndi mau awa, nasinkhasinkha kulonjera uku nkutani.


Ndipo pompenyetsetsa iye ndi kuopa, anati, Nchiyani, Mbuye? Ndipo anati kwa iye, Mapemphero ako ndi zachifundo zako zinakwera zikhala chikumbutso pamaso pa Mulungu.


Ndipo pamene ndinamuona Iye, ndinagwa pa mapazi ake ngati wakufa; ndipo anaika dzanja lake lamanja pa ine, nati, Usaope, Ine ndine Woyamba ndi Wotsiriza,


Nati Manowa kwa mkazi wake, Tidzafa ndithu pakuti taona Mulungu.


Pamenepo Gideoni anaona kuti ndiye mthenga wa Yehova, nati Gideoni, Tsoka ine, Yehova Mulungu! Popeza ndaona mthenga wa Yehova maso ndi maso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa