Levitiko 6:9 - Buku Lopatulika9 Uza Aroni ndi ana ake, ndi kuti, Chilamulo cha nsembe yopsereza ndi ichi: nsembe yopsereza izikhala pa nkhuni za paguwa la nsembe usiku wonse kufikira m'mawa; ndipo moto wa paguwa la nsembe uziyakabe pamenepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Uza Aroni ndi ana ake, ndi kuti, Chilamulo cha nsembe yopsereza ndi ichi: nsembe yopsereza izikhala pa nkhuni za pa guwa la nsembe usiku wonse kufikira m'mawa; ndipo moto wa pa guwa la nsembe uziyakabe pamenepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Ulamule Aroni pamodzi ndi ana ake kuti, ‘Lamulo la nsembe yopsereza kwathunthu ndi ili: nsembeyo izikhala pa moto pa guwa usiku wonse mpaka m'maŵa, ndipo moto wapaguwapowo uzikhala uli chiyakire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Lamula Aaroni ndi ana ake kuti, ‘Lamulo la nsembe yopsereza ndi ili: Nsembe yopserezayo izikhala pa moto pa guwa usiku wonse mpaka mmawa, ndipo moto wa paguwapo uzikhala ukuyaka nthawi zonse. Onani mutuwo |