Levitiko 3:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo chopereka chake chikakhala nkhosa kapena mbuzi, kuti ikhale nsembe yoyamika ya kwa Yehova; ingakhale yaimuna kapena yaikazi, azibwera nayo yopanda chilema; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo chopereka chake chikakhala nkhosa kapena mbuzi, kuti ikhale nsembe yoyamika ya kwa Yehova; ingakhale yaimuna kapena yaikazi, azibwera nayo yopanda chilema; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Ngati munthu apereka nsembe yachiyanjano kwa Chauta, nsembe yake ikakhala nkhosa yamphongo kapena yaikazi, ikhale yopanda chilema. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “ ‘Ngati munthu apereka nsembe ya chiyanjano kwa Yehova, choperekacho chikhale nkhosa yayimuna kapena yayikazi yopanda chilema. Onani mutuwo |