Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 27:4 - Buku Lopatulika

4 Koma akakhala wamkazi, umuyesere wa masekeli makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Koma akakhala wamkazi, umuyesere wa masekeli makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Munthu wake akakhala wamkazi, mtengo wake ukhale wokwana masekeli asiliva makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ndipo ngati ndi wamkazi, mtengo wake ukhale masekeli makumi atatu.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 27:4
5 Mawu Ofanana  

Ukayesa wamwamuna wa zaka makumi awiri kufikira wina wa zaka makumi asanu ndi limodzi, uziwayesera a masekeli makumi asanu a siliva, monga mwa sekeli wa malo opatulika.


Akakhala munthu wa zaka zisanu kufikira wina wa zaka makumi awiri uwayesere, wamwamuna wa masekeli makumi awiri, ndi wamkazi wa masekeli khumi.


nati, Mufuna kundipatsa chiyani, ndipo ine ndidzampereka Iye kwa inu? Ndipo iwo anamwerengera iye ndalama zasiliva makumi atatu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa