Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 27:5 - Buku Lopatulika

5 Akakhala munthu wa zaka zisanu kufikira wina wa zaka makumi awiri uwayesere, wamwamuna wa masekeli makumi awiri, ndi wamkazi wa masekeli khumi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Akakhala munthu wa zaka zisanu kufikira wina wa zaka makumi awiri uwayesere, wamwamuna wa masekeli makumi awiri, ndi wamkazi wa masekeli khumi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Akakhala munthu wa zaka zisanu mpaka zaka makumi aŵiri, mtengo wake ukhale wokwana masekeli asiliva makumi aŵiri pa munthu wamwamuna, ndipo khumi pa munthu wamkazi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Mtengo wa munthu wamwamuna wa zaka zapakati pa zisanu ndi makumi awiri ukhale masekeli makumi awiri ndipo munthu wamkazi ukhale masekeli khumi.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 27:5
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anapita pamenepo Amidiyani a malonda: ndipo anamtulutsa namkweza Yosefe m'dzenjemo, namgulitsa kwa Aismaele ndi masekeli a siliva makumi awiri; ndipo ananka naye Yosefe ku Ejipito.


Koma akakhala wamkazi, umuyesere wa masekeli makumi atatu.


Akakhala mwana wa mwezi umodzi kufikira zaka zisanu, uziwayesera wamwamuna wa masekeli asanu a siliva, ndi wamkazi wa masekeli atatu a siliva.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa