Levitiko 2:12 - Buku Lopatulika12 Monga chopereka cha zipatso zoyamba muzipereka izi kwa Yehova: koma asazifukize paguwa la nsembe zichite fungo lokoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Monga chopereka cha zipatso zoyamba muzipereka izi kwa Yehova: koma asazifukize pa guwa la nsembe zichite fungo lokoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ziŵirizo ungathe kubwera nazo ngati nsembe ya zokolola zoyambirira zopereka kwa Chauta. Koma usazitenthere pa guwa kuti zipereke fungo lonunkhira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ziwirizi ungathe kubwera nazo kwa Yehova ngati chopereka cha zokolola zoyambirira. Koma usazitenthe pa guwa kuti zikhale fungo lokomera Yehova. Onani mutuwo |