Levitiko 11:7 - Buku Lopatulika7 Ndi nkhumba, popeza igawanika chiboda, nikhala yogawanikadi chiboda, koma yosabzikula, muiyese yodetsedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndi nkhumba, popeza igawanika chiboda, nikhala yogawanikadi chiboda, koma yosabzikula, muiyese yodetsedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Nkhumba: imeneyi njonyansa kwa inu, chifukwa ngakhale ziboda zake nzogaŵikana ndipo mapazi ake ngogaŵikananso, koma siibzikula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Nkhumba simabzikula ngakhale ili ndi zipondero zogawikana. Choncho ndi yodetsedwa, musadye. Onani mutuwo |