Levitiko 11:6 - Buku Lopatulika6 Ndi kalulu, popeza abzikula koma wosagawanika chiboda, mumuyese wodetsedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndi kalulu, popeza abzikula koma wosagawanika chiboda, mumuyese wodetsedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Kalulu: ameneyu ndi wonyansa kwa inu, chifukwa ngakhale amabzikula, ziboda zake nzosagaŵikana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Inanso ndi kalulu, ngakhale amabzikula, zipondero zake nʼzosagawikana. Choncho ndi wodetsedwa, musadye. Onani mutuwo |