Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Levitiko 10:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Yehova ananena ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Yehova ananena ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Tsono Chauta adalankhula ndi Aroni namuuza kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Pambuyo pake Yehova anayankhula ndi Aaroni nati,

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 10:8
3 Mawu Ofanana  

Masiku ambiri tsono Israele anakhala wopanda Mulungu woonayo, ndi wopanda wansembe wakuphunzitsa, ndi wopanda chilamulo;


Ndipo musatuluka pakhomo pa chihema chokomanako, kuti mungafe, pakuti mafuta odzoza a Yehova ali pa inu. Ndipo anachita monga mwa mau a Mose.


Usamamwa vinyo, kapena choledzeretsa, iwe ndi ana ako omwe, m'mene mulowa m'chihema chokomanako, kuti mungafe; likhale lemba losatha mwa mibadwo yanu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa