Levitiko 1:2 - Buku Lopatulika2 Lankhula ndi ana a Israele, nunene nao, Aliyense mwa inu akabwera nacho chopereka cha kwa Yehova, muzibwera nacho chopereka chanu chikhale cha zoweta, cha ng'ombe, kapena cha nkhosa, kapena cha mbuzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Lankhula ndi ana a Israele, nunene nao, Aliyense mwa inu akabwera nacho chopereka cha kwa Yehova, muzibwera nacho chopereka chanu chikhale cha zoweta, cha ng'ombe, kapena cha nkhosa, kapena cha mbuzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Uza Aisraele kuti, ‘Munthu aliyense akamabwera ndi chopereka kwa Chauta, azitenga ng'ombe kapena nkhosa kapena mbuzi.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Aliyense wa inu ngati abwera ndi nsembe kwa Yehova kuchokera pa ziweto zake, choperekacho chikhale ngʼombe, nkhosa kapena mbuzi. Onani mutuwo |