Hoseya 7:3 - Buku Lopatulika3 Akondweretsa mfumu ndi zoipa zao, ndi akalonga ndi mabodza ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Akondweretsa mfumu ndi zoipa zao, ndi akalonga ndi mabodza ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Anthu amakopa mfumu ndi makhalidwe ao oipa, nduna zake amazinyenga ndi mabodza ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 “Anthuwa amasangalatsa mfumu ndi zoyipa zawozo, akalonga amasekerera mabodza awo. Onani mutuwo |