Hoseya 7:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo sanafuulire kwa Ine ndi mtima wao, koma alira pakama pao, asonkhanira tirigu ndi vinyo, apikisana ndi Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo sanafuulire kwa Ine ndi mtima wao, koma alira pakama pao, asonkhanira tirigu ndi vinyo, apikisana ndi Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Kulira kwao kwa Ine nkwabodza, amalira ali gone pa bedi. Amadzichekacheka ngati akunja chifukwa chofuna chakudya ndi chakumwa, komabe amandipandukira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Iwo salirira kwa Ine kuchokera pansi pa mtima, koma amalira mofuwula ali pa bedi pawo. Amadzichekacheka chifukwa chofuna tirigu ndi vinyo watsopano, koma amandifulatira. Onani mutuwo |