Hoseya 7:12 - Buku Lopatulika12 Pamene amuka ndidzawayalira ukonde wanga, ndidzawagwetsa ngati mbalame za m'mlengalenga, ndidzawalanga monga udamva msonkhano wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pamene amuka ndidzawayalira ukonde wanga, ndidzawagwetsa ngati mbalame za m'mlengalenga, ndidzawalanga monga udamva msonkhano wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Kulikonse kumene amapita, ndidzaŵatchera ukonde. Ndidzaŵagwetsa pansi ngati mbalame zamumlengalenga. Ndidzaŵalanga chifukwa cha zolakwa zao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Akamadzapita, ndidzawakola ndi ukonde wanga; ndidzawagwetsa pansi ngati mbalame zamumlengalenga. Ndikadzamva kuti asonkhana pamodzi ndidzawakola. Onani mutuwo |