Hoseya 4:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo udzakhumudwa usana, ndi mneneri yemwe adzakhumudwa pamodzi ndi iwe usiku; ndipo ndidzaononga mai wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo udzakhumudwa usana, ndi mneneri yemwe adzakhumudwa pamodzi ndi iwe usiku; ndipo ndidzaononga mai wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mumakhumudwa usana ndi usiku, ndipo aneneri nawonso amachita chimodzimodzi, motero ndidzaononga Israele mai wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mumapunthwa usana ndi usiku ndipo aneneri amapunthwa nanu pamodzi. Choncho ndidzawononga amayi anu. Onani mutuwo |