Hoseya 2:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti mai wao anachita chigololo; iye amene anali ndi pakati pa iwo anachita chamanyazi; pakuti anati, Ndidzatsata ondikondawo, akundipatsa ine chakudya changa, ndi madzi anga, ubweya wanga, ndi thonje langa, mafuta anga, ndi chakumwa changa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti mai wao anachita chigololo; iye amene anali ndi pakati pa iwo anachita chamanyazi; pakuti anati, Ndidzatsata ondikondawo, akundipatsa ine chakudya changa, ndi madzi anga, ubweya wanga, ndi thonje langa, mafuta anga, ndi chakumwa changa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Paja mai wao ndi wachiwerewere. Amene adaŵabala ankachita zomvetsa manyazi. Ankati, ‘Nditsatira zibwenzi zanga zimene zimandipatsa chakudya ndi madzi, ubweya ndi thonje, mafuta ndi vinyo.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Amayi awo akhala akuchita zachiwerewere ndipo anawabereka anawo akuchita zinthu zochititsa manyazi. Iwo anati, ‘Ine ndidzatsatira zibwenzi zanga, zimene zimandipatsa chakudya ndi madzi, ubweya ndi thonje, mafuta ndi chakumwa.’ Onani mutuwo |