Hoseya 2:6 - Buku Lopatulika6 Chifukwa chake taonani, ndidzatchinga njira yako ndi minga, ndipo ndidzammangira mpanda, kuti asapeze mabande ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Chifukwa chake taonani, ndidzatchinga njira yako ndi minga, ndipo ndidzammangira mpanda, kuti asapeze mabande ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Nchifukwa chake njira yake ndidzaitseka ndi minga. Ndidzamuzinga ndi khoma, kuti asayendenso m'njira zake zakale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Choncho njira yake ndidzayitseka ndi minga; ndidzamuzinga ndi khoma kotero kuti sadzapezanso njira yotulukira. Onani mutuwo |