Hoseya 2:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo ndidzadzibzalira iye m'nthaka, ndipo ndidzachitira chifundo Wosachitidwa-chifundo; ndipo ndidzati kwa Si-anthu-anga, Muli anthu anga; ndipo iwo adzati, Ndinu Mulungu wathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo ndidzadzibzalira iye m'nthaka, ndipo ndidzachitira chifundo Wosachitidwa-chifundo; ndipo ndidzati kwa Si-anthu-anga, Muli anthu anga; ndipo iwo adzati, Ndinu Mulungu wathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Israele ndidzamubzala m'dziko kuti akhale wanga. Ndidzaonetsa chikondi kwa ‘Sakondedwa’ uja. Anthu amene ndinkaŵatchula ‘Si-anthu-anga,’ ndidzaŵauza kuti, ‘Ndinu anthu anga.’ Ndipo iwo adzanena kuti, ‘Ndinu Mulungu wathu.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndidzadzala Israeli mʼdziko kuti akhale wanga: ndidzaonetsa chikondi changa kwa anthu amene ndinkawatchula dzina loti, ‘Sakondedwa.’ Ndidzawawuza amene ndinkawatchula dzina loti, ‘Si anthu anga,’ kuti, ‘Ndinu anthu wanga;’ ndipo adzanena kuti, ‘ndinu Mulungu wathu,’ ” Onani mutuwo |