Hoseya 2:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo ndidzakutomera ukhale wanga kosatha, inde ndidzakutomera ukhale wanga m'chilungamo, ndi m'chiweruzo, ndi mu ukoma mtima, ndi m'chifundo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo ndidzakutomera ukhale wanga kosatha, inde ndidzakutomera ukhale wanga m'chilungamo, ndi m'chiweruzo, ndi m'ukoma mtima, ndi m'chifundo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Iwe Israele, ndidzakutomera kuti ukhale mkazi wanga mpaka muyaya. Ndidzakutomera mwaungwiro, mwachilungamo, mwa chikondi chosasinthika, ndiponso mwachifundo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ndidzakutomera kuti ukhale mkazi wanga mpaka muyaya; ndidzakutomera mwachilungamo, mwaungwiro, mwachikondi ndi mwachifundo. Onani mutuwo |