Hoseya 13:8 - Buku Lopatulika8 Ndidzakomana nao ngati chimbalangondo chochilanda ana ake, ndi kung'amba chokuta mtima wao; ndi pomwepo ndidzawalusira ngati mkango; chilombo chidzawamwetula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndidzakomana nao ngati chimbalangondo chochilanda ana ake, ndi kung'amba chokuta mtima wao; ndi pomwepo ndidzawalusira ngati mkango; chilombo chidzawamwetula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ndidzaŵambwandira ngati chimbalangondo cholandidwa ana. Ndidzathyola nthiti zao, ndipo ndidzaŵamwamwata pomwepo ngati mkango, ndidzaŵankhanthula ngati chilombo choopsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ngati chimbalangondo cholandidwa ana ake, ndidzawambwandira ndi kuwathyolathyola. Ndidzawapwepweta ngati mkango; chirombo chakuthengo chidzawakhadzula. Onani mutuwo |